2 Samueli 19:29 - Buku Lopatulika29 Ndipo mfumu inanena naye, Ulikulankhulanso bwanji za zinthu zako? Ine ndikuti, Iwe ndi Ziba mugawe dzikolo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201429 Ndipo mfumu inanena naye, Ulikulankhulanso bwanji za zinthu zako? Ine ndikuti, Iwe ndi Ziba mugawe dzikolo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa29 Apo mfumu idati, “Basi ndamva usaonjezenso mau ena ai. Ine ndikufuna kuti iwe ndi Ziba mugaŵane chuma cha Saulo.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero29 Mfumu inayankha kuti, “Uneneranji zambiri? Ine ndikulamula kuti iwe ndi Ziba mugawane minda.” Onani mutuwo |