2 Samueli 19:26 - Buku Lopatulika26 Ndipo anayankha, Mbuye wanga mfumu, mnyamata wanga anandinyenga; pakuti mnyamata wanu ndinati, Ndidzadzimangira bulu kuti ndiberekekepo ndi kupita ndi mfumu, pakuti mnyamata wanu ndili wopunduka. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201426 Ndipo anayankha, Mbuye wanga mfumu, mnyamata wanga anandinyenga; pakuti mnyamata wanu ndinati, Ndidzadzimangira bulu kuti ndiberekekepo ndi kupita ndi mfumu, pakuti mnyamata wanu ndili wopunduka. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa26 Mefiboseti adayankha kuti, “Ine mbuyanga mfumu, adaandilakwitsa ndi wantchito wanga. Kapolo wanune wantchitoyo ndidamuuza bwinobwino kuti, ‘Undimangire chishalo pa bulu kuti ndikwere, ndipite nawo limodzi amfumu,’ poti paja ine kapolo wanu ndine wolumala. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero26 Iye anayankha kuti, “Mbuye wanga mfumu, pakuti ine wantchito wanu ndine wolumala. Ndinati, ‘Andikonzere chishalo cha bulu wanga ndipo ndidzakwera kuti ndipite ndi mfumu.’ Koma Ziba wantchito wanga anandilakwitsa. Onani mutuwo |