2 Samueli 19:20 - Buku Lopatulika20 Pakuti mnyamata wanu ndidziwa kuti ndinachimwa; chifukwa chake, onani, ndinadza lero, ndine woyamba wa nyumba yonse ya Yosefe kutsika kuti ndikomane ndi mbuye wanga mfumu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201420 Pakuti mnyamata wanu ndidziwa kuti ndinachimwa; chifukwa chake, onani, ndinadza lero, ndine woyamba wa nyumba yonse ya Yosefe kutsika kuti ndikomane ndi mbuye wanga mfumu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa20 Ine kapolo wanu ndikudziŵa kuti ndidalakwa. Nchifukwa chake mukuwona kuti ndabwera lero lino, ndipo m'banja lonse la Yosefe, ndayambira ndine kubwera kudzakuchingamirani inu mbuyanga mfumu.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero20 Pakuti ine mtumiki wanu ndazindikira kuti ndachimwa. Koma lero ndabwera ngati woyamba wa nyumba ya Yosefe yonse kudzakumana nanu mbuye wanga mfumu.” Onani mutuwo |