2 Samueli 19:18 - Buku Lopatulika18 Ndipo ngalawa yakuolotsera inaoloka kuti akatenge banja la mfumu ndi kuchita chomkomera. Ndipo Simei mwana wa Gera anagwa pansi pamaso pa mfumu pakuoloka iye pa Yordani. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201418 Ndipo ngalawa yakuolotsera inaoloka kuti akatenge banja la mfumu ndi kuchita chomkomera. Ndipo Simei mwana wa Gera anagwa pansi pamaso pa mfumu pakuoloka iye pa Yordani. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa18 Ndipo adaolotsa onse a m'banja la mfumu, nachita zonse zokondweretsa mfumuyo. Tsono pamene mfumu Davide anali pafupi kuwoloka Yordani, Simei mwana wa Gera, adadzigwetsa pansi pamaso pa mfumuyo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero18 Iwo anawoloka mtsinje kukatenga banja lonse la mfumu ndi kuchita zonse zimene mfumuyo imafuna. Pamene Simei mwana wa Gera anawoloka Yorodani, anagwa pansi chafufumimba pamaso pa mfumu, Onani mutuwo |