2 Samueli 19:13 - Buku Lopatulika13 Ndipo munene ndi Amasa, Suli fupa langa ndi mnofu wanga kodi? Mulungu andilange naonjezepo ngati sudzakhala chikhalire kazembe wa khamu la ankhondo pamaso panga, m'malo mwa Yowabu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Ndipo munene ndi Amasa, Suli fupa langa ndi mnofu wanga kodi? Mulungu andilange naonjezepo ngati sudzakhala chikhalire kazembe wa khamu la ankhondo pamaso panga, m'malo mwa Yowabu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Ndipo mukauze Amasa mau anga oti, ‘Kodi iwe, sindiwe mbale wanga weniweni?’ Ndithu Mulungu andilange, mpaka ndife ndithu, ngati sindikuika iwe kuti ukhale mkulu wankhondo m'malo mwa Yowabu kuyambira tsopano lino.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Ndipo munene kwa Amasa, ‘Kodi iwe si mʼbale wanga weniweni? Mulungu andilange, andilange kwambiri ngati kuyambira tsopano sukhala mtsogoleri wa ankhondo anga kulowa mʼmalo mwa Yowabu.’ ” Onani mutuwo |