2 Samueli 19:12 - Buku Lopatulika12 Inu ndinu abale anga, muli fupa langa ndi mnofu wanga; chifukwa ninji tsono muli am'mbuyo koposa onse kubwera nayo mfumu? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Inu ndinu abale anga, muli fupa langa ndi mnofu wanga; chifukwa ninji tsono muli am'mbuyo koposa onse kubwera nayo mfumu? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Inu ndinu abale anga enieni. Chifukwa chiyani inuyo mukufuna kukhala otsirizira pakuiitananso mfumu?’ Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 Inu ndinu abale anga enieni, mafupa anga ndi mnofu wanga. Nʼchifukwa chiyani inuyo mukukhala otsiriza kubweretsa mfumu?’ Onani mutuwo |