2 Samueli 19:10 - Buku Lopatulika10 Ndipo Abisalomu amene tinamdzoza mfumu yathu anafa kunkhondo. Chifukwa chake tsono mulekeranji kunena mau akuti abwere nayo mfumuyo? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Ndipo Abisalomu amene tinamdzoza mfumu yathu anafa kunkhondo. Chifukwa chake tsono mulekeranji kunena mau akuti abwere nayo mfumuyo? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Koma Abisalomuyo amene ife tidamdzoza kuti akhale mfumu yathu, adafa ku nkhondo. Chifukwa chiyani tsono simukunena kanthu zokatenga mfumu Davide kuti abwerenso?” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Ndipo Abisalomu amene ife tinamudzoza kuti atilamulire wafa pa nkhondo. Tsono nʼchifukwa chiyani simukunena kanthu za kubweretsanso mfumu?” Onani mutuwo |