2 Samueli 18:8 - Buku Lopatulika8 Pakuti nkhondo inatanda padziko lonse, ndipo tsiku lomwelo nkhalango inaononga anthu akuposa amene anaonongeka ndi lupanga. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Pakuti nkhondo inatanda pa dziko lonse, ndipo tsiku lomwelo nkhalango inaononga anthu akuposa amene anaonongeka ndi lupanga. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Nkhondo idafalikira m'dziko lonselo, ndipo zoopsa zam'nkhalango zidapha anthu ambiri kuposa anthu ophedwa ndi lupanga. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Nkhondo inafalikira ku madera onse akumidzi ndipo anthu akufa chifukwa cha zoopsa za mʼnkhalango anali ambiri tsiku limenelo kuposa akufa ndi lupanga. Onani mutuwo |