2 Samueli 18:7 - Buku Lopatulika7 Ndipo anthu a Israele anakanthidwa pamenepo pamaso pa anyamata a Davide, ndipo kunali kuwapha kwakukulu kumeneko tsiku lomwelo, anthu zikwi makumi awiri. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Ndipo anthu a Israele anakanthidwa pamenepo pamaso pa anyamata a Davide, ndipo kunali kuwapha kwakukulu kumeneko tsiku lomwelo, anthu zikwi makumi awiri. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Aisraele adagonjetsedwa kumeneko ndi ankhondo a Davide. Motero tsiku limenelo adaphedwa anthu ambiri okwanira 20,000 onse pamodzi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Aisraeli anagonjetsedwa kumeneko ndi ankhondo a Davide. Tsiku limenelo anaphedwa anthu okwanira 20,000. Onani mutuwo |