Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




2 Samueli 18:30 - Buku Lopatulika

30 Ndipo mfumu inati, Patuka nuime apa. Napatuka, naimapo.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

30 Ndipo mfumu inati, Patuka nuime apa. Napatuka, naimapo.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

30 Pompo mfumu idati, “Patuka, kaime apo.” Iye adapatuka nakaima potero.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

30 Mfumu inati, “Ima apo ndipo udikire.” Kotero iye anapita pa mbali nayima pamenepo.

Onani mutuwo Koperani




2 Samueli 18:30
2 Mawu Ofanana  

Ndipo mfumu inati, Kodi mnyamatayo Abisalomu ali bwino? Ahimaazi nayankha, Pamene Yowabu anatumiza mnyamata wa mfumu, ndiye ine mnyamata wanu, ndinaona piringupiringu, koma sindinadziwe ngati kutani.


Ndipo onani, Mkusiyo anafika, nati, Mau akuuza mbuye wanga mfumu; pakuti Yehova anabwezera chilango lero onse akuukira inu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa