2 Samueli 18:16 - Buku Lopatulika16 Ndipo Yowabu analiza lipenga, ndipo anthu anabwerera naleka kupirikitsa Aisraele; pakuti Yowabu analetsa anthuwo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201416 Ndipo Yowabu analiza lipenga, ndipo anthu anabwerera naleka kupirikitsa Aisraele; pakuti Yowabu analetsa anthuwo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa16 Pambuyo pake Yowabu adaliza lipenga loletsa nkhondo, ndipo ankhondo ake adabwerako kumene ankalondola Aisraele kuja. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero16 Kenaka Yowabu analiza lipenga ndipo asilikali analeka kuthamangitsa Israeli pakuti Yowabu anawaletsa. Onani mutuwo |