2 Samueli 18:14 - Buku Lopatulika14 Pomwepo Yowabu anati, Sindiyenera kuchedwa nawe. Natenga mikondo itatu nagwaza nayo mtima wa Abisalomu alikukhala wamoyo pakati pa mtengowo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 Pomwepo Yowabu anati, Sindiyenera kuchedwa nawe. Natenga mikondo itatu nagwaza nayo mtima wa Abisalomu alikukhala wamoyo pakati pa mtengowo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 Apo Yowabu adati, “Ukunditayitsa nthaŵi!” Ndipo adatenga mikondo itatu m'manja mwake, nakabaya Abisalomu m'chifuŵa asanafe, akali lendee mu mtengo wa thunduwo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 Yowabu anati, “Ine sinditayanso nthawi ndi iwe.” Ndipo anatenga mikondo itatu mʼmanja mwake ndipo anabaya pamtima pa Abisalomu, Abisalomuyo akanali ndi moyo pa mtengo wa thundu. Onani mutuwo |