Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




2 Samueli 18:13 - Buku Lopatulika

13 Ndikadachita chonyenga pa moyo wake, palibe mlandu ubisika kwa mfumu; ndipo inu nomwe mukadanditsutsa.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

13 Ndikadachita chonyenga pa moyo wake, palibe mlandu ubisika kwa mfumu; ndipo inu nomwe mukadanditsutsa.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

13 Bwenzi nditanyoza mau a mfumuwo, pomupha mwana wake, ndipo zikadadziŵika, poti palibe kanthu kobisika pamaso pa mfumu, ndipo inu nomwe simukadanditeteza.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

13 Ndipo sindikanayika moyo wanga pa chiswe pakuti palibe chimene chimabisika pamaso pa mfumu komanso inu simukanditeteza.”

Onani mutuwo Koperani




2 Samueli 18:13
4 Mawu Ofanana  

Ndipo palibe cholembedwa chosaonekera pamaso pake, koma zonse zikhala za pambalambanda ndi zovundukuka pamaso pake pa Iye amene tichita naye.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa