2 Samueli 18:10 - Buku Lopatulika10 Ndipo munthu wina anamuona, nauza Yowabu, nati, Onani, ndaona Abisalomu ali lende pathundu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Ndipo munthu wina anamuona, nauza Yowabu, nati, Onani, ndaona Abisalomu ali lende pathundu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Munthu wina ataona zimenezo, adauza Yowabu kuti, “Ndamuwona Abisalomu ali lendee mu mtengo wa thundu.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Mmodzi mwa asilikali ataona zimenezi, anamuwuza Yowabu kuti, “Ine ndamuona Abisalomu ali lende mu mtengo wa thundu.” Onani mutuwo |