2 Samueli 18:1 - Buku Lopatulika1 Ndipo Davide anawerenga anthu amene anali naye, nawaikira atsogoleri a zikwi ndi atsogoleri a mazana. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Ndipo Davide anawerenga anthu amene anali naye, nawaikira atsogoleri a zikwi ndi atsogoleri a mazana. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Pambuyo pake Davide adasonkhanitsa anthu amene anali naye kuti aŵagaŵe m'magulu, ndipo adaŵaikira atsogoleri, ena olamulira anthu zikwi, ena olamulira anthu mazana. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Davide anasonkhanitsa anthu amene anali naye ndipo anasankha atsogoleri ena olamulira ankhondo 1,000 ndi ena olamulira ankhondo 100. Onani mutuwo |