2 Samueli 18:1 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Davide anasonkhanitsa anthu amene anali naye ndipo anasankha atsogoleri ena olamulira ankhondo 1,000 ndi ena olamulira ankhondo 100. Onani mutuwoBuku Lopatulika1 Ndipo Davide anawerenga anthu amene anali naye, nawaikira atsogoleri a zikwi ndi atsogoleri a mazana. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Ndipo Davide anawerenga anthu amene anali naye, nawaikira atsogoleri a zikwi ndi atsogoleri a mazana. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Pambuyo pake Davide adasonkhanitsa anthu amene anali naye kuti aŵagaŵe m'magulu, ndipo adaŵaikira atsogoleri, ena olamulira anthu zikwi, ena olamulira anthu mazana. Onani mutuwo |