Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




2 Samueli 17:24 - Buku Lopatulika

24 Ndipo Davide anafika ku Mahanaimu. Abisalomu naoloka Yordani, iye ndi anthu onse a Israele pamodzi naye.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

24 Ndipo Davide anafika ku Mahanaimu. Abisalomu naoloka Yordani, iye ndi anthu onse a Israele pamodzi naye.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

24 Davide adafika ku Mahanaimu. Abisalomu adaoloka Yordani pamodzi ndi Aisraele onse aja.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

24 Davide anapita ku Mahanaimu, ndipo Abisalomu anawoloka Yorodani pamodzi ndi ankhondo ena onse a Israeli.

Onani mutuwo Koperani




2 Samueli 17:24
5 Mawu Ofanana  

sindiyenera zazing'ono za zifundo zonse, ndi zoona zonse, zimene mwamchitira kapolo wanu: chifukwa ndindodo yanga ndinaoloka pa Yordani uyu; ndipo tsopano ndili makamu awiri.


Pamene Yakobo anawaona anati, Ili ndi khamu la Mulungu: ndipo anatcha pamenepo dzina lake Mahanaimu.


Koma Abinere, mwana wa Nere, kazembe wa khamu la ankhondo a Saulo anatenga Isiboseti mwana wa Saulo, namuolotsa nanka naye ku Mahanaimu;


Anati, Bwera, bwera, Msulamiwe; bwera, bwera, tiyang'ane pa iwe. Muyang'aniranji pa Msulami, ngati pa masewero akuguba?


ndi kuyambira Hesiboni mpaka Ramati-Mizipe, ndi Betonimu; ndi kuyambira Mahanaimu mpaka malire a Debiri;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa