2 Samueli 15:9 - Buku Lopatulika9 Ndipo mfumu inanena naye, Muka ndi mtendere. Chomwecho ananyamuka, nanka ku Hebroni. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Ndipo mfumu inanena naye, Muka ndi mtendere. Chomwecho ananyamuka, nanka ku Hebroni. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Apo mfumu idamuuza kuti, “Upite ndi mtendere.” Choncho Abisalomu adanyamuka napita ku Hebroni. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Mfumu inati kwa iye, “Pita mu mtendere” Kotero iye anapita ku Hebroni. Onani mutuwo |