2 Samueli 15:15 - Buku Lopatulika15 Ndipo anyamata a mfumu ananena kwa mfumu, Onani, monga mwa zonse mbuye wathu mfumu adzasankha, anyamata anu ndife. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201415 Ndipo anyamata a mfumu ananena kwa mfumu, Onani, monga mwa zonse mbuye wathu mfumu adzasankha, anyamata anu ndife. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa15 Apo nduna za mfumu zija zidauza mfumu kuti, “Amfumu, ife ankhondo anu tili okonzeka kuchita chinthu chilichonse chimene inu mungachitsimikize kuchita.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero15 Akuluakulu a mfumu anamuyankha kuti, “Antchito anu ndi okonzeka kuchita chilichonse chimene mbuye wathu mfumu mukufuna kuchita.” Onani mutuwo |