2 Samueli 14:18 - Buku Lopatulika18 Pamenepo mfumu inayankha, ninena naye mkaziyo, Usandibisire kanthu ka zimene ndidzakufunsa iwe. Mkaziyo nati, Mbuye wanga mfumu anene. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201418 Pamenepo mfumu inayankha, ninena naye mkaziyo, Usandibisire kanthu ka zimene ndidzakufunsa iwe. Mkaziyo nati, Mbuye wanga mfumu anene. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa18 Apo mfumu idamuyankha mkaziyo kuti, “Musandibisire kanthu kalikonse pa zimene ndikufunseni.” Mkazi uja adati, “Ai ndithu, mbuyanga mfumu sindikubisirani.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero18 Kenaka mfumu inati kwa mkaziyo, “Usandibisire chilichonse pondiyankha chimene ndidzakufunsa.” Mkaziyo anati, “Mbuye wanga mfumu yankhulani.” Onani mutuwo |
Ndipo mfumuyo inati, Kodi Yowabu adziwana ndi iwe mwa izi zonse? Mkaziyo nayankha nati, Pali moyo wanu mbuye wanga mfumu, palibe kulewa ku dzanja lamanja, kapena kulamanzere kwa zonse mudazinena mbuye wanga mfumu; pakuti mnyamata wanu Yowabu ndiye anandiuza, naika mau onse awa m'kamwa mwa mdzakazi wanu.