2 Samueli 13:27 - Buku Lopatulika27 Koma Abisalomu anaiumirira iyo, nilola kuti Aminoni ndi ana aamuna onse a mfumu apite naye. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201427 Koma Abisalomu anaiumirira iyo, nilola kuti Aminoni ndi ana amuna onse a mfumu apite naye. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa27 Koma Abisalomu adamkakamiza ndithu mpaka Davide adalola kuti Aminoni pamodzi ndi ana onse aamuna a mfumu apite nao. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero27 Koma Abisalomu anamuwumiriza, kotero analola kuti Amnoni pamodzi ndi ana onse a mfumu apite naye. Onani mutuwo |