2 Samueli 13:11 - Buku Lopatulika11 Ndipo pamene anabwera nato pafupi kuti adye, iye anamgwira, nanena naye, Idza nugone nane, mlongo wanga. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Ndipo pamene anabwera nato pafupi kuti adye, iye anamgwira, nanena naye, Idza nugone nane, mlongo wanga. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Koma atafika nacho chakudyacho pafupi ndi Aminoni kuti adye, Aminoni adamgwira Tamara, namuuza kuti, “Bwera ugone nane, iwe Tamara.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Koma atabweretsa kwa iye kuti adye, anamugwira ndipo anati, “Bwera ugone nane, iwe mlongo wanga.” Onani mutuwo |