Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




2 Samueli 13:11 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

11 Koma atabweretsa kwa iye kuti adye, anamugwira ndipo anati, “Bwera ugone nane, iwe mlongo wanga.”

Onani mutuwo Koperani

Buku Lopatulika

11 Ndipo pamene anabwera nato pafupi kuti adye, iye anamgwira, nanena naye, Idza nugone nane, mlongo wanga.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

11 Ndipo pamene anabwera nato pafupi kuti adye, iye anamgwira, nanena naye, Idza nugone nane, mlongo wanga.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

11 Koma atafika nacho chakudyacho pafupi ndi Aminoni kuti adye, Aminoni adamgwira Tamara, namuuza kuti, “Bwera ugone nane, iwe Tamara.”

Onani mutuwo Koperani




2 Samueli 13:11
4 Mawu Ofanana  

Patapita kanthawi, mkazi wa mbuye wake anayamba kusirira Yosefe nati, “Bwanji ugone nane!”


Kenaka Amnoni anati kwa Tamara, “Bweretsa chakudya kuno, ku chipinda changa chogona kuti ndidye chili mʼmanja mwako.” Ndipo Tamara anatenga buledi amene anapanga ndi kubwera naye kwa mlongo wake ku chipinda chake.


Ena amachita chigololo ndi akazi a anzawo, ndipo ena, mopanda manyazi, amayipitsa mkazi wa mwana wawo. Palinso ena amene amayipitsa alongo awo, ana aakazi a abambo awo.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa