Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




2 Samueli 12:28 - Buku Lopatulika

28 Chifukwa chake tsono musonkhanitse anthu otsalawo, nimumangire mzindawo zithando, muulande; kuti ine ndingalande mzindawo, ndipo ungatchedwe ndi dzina langa.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

28 Chifukwa chake tsono musonkhanitse anthu otsalawo, nimumangire mudziwo zithando, muulande; kuti ine ndingalande mudziwo, ndipo ungatchedwe ndi dzina langa.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

28 Tsono inu musonkhanitse ankhondo onse otsala, ndipo bwerani mudzauzinge ndi zithando mzindawo ndi kuulanda, kuwopa kuti ine ndikalanda mzindawo, ungamatchedwe dzina langa.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

28 Ndipo tsopano sonkhanitsani asilikali onse ndipo muzungulire mzindawo ndi kuwulanda.”

Onani mutuwo Koperani




2 Samueli 12:28
3 Mawu Ofanana  

Yowabu natumiza mithenga kwa Davide nati, Ndaponyana ndi Raba, inde ndalanda mzinda wa pamadzi.


Ndipo Davide anasonkhanitsa anthu onse, napita ku Raba, naponyana nao, naulanda.


Iye wolankhula zochokera kwa iye yekha afuna ulemu wa mwini yekha. Iye wakufuna ulemu wa Iye amene anamtuma, yemweyu ali woona, ndipo mwa Iye mulibe chosalungama.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa