2 Samueli 12:27 - Buku Lopatulika27 Yowabu natumiza mithenga kwa Davide nati, Ndaponyana ndi Raba, inde ndalanda mzinda wa pamadzi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201427 Yowabu natumiza mithenga kwa Davide nati, Ndaponyana ndi Raba, inde ndalanda mudzi wa pamadzi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa27 Adatuma amithenga kwa Davide kukamuuza kuti, “Ndauthira nkhondo mzinda wa Raba, ndipo ndalanda nkhokwe yake ya madzi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero27 Ndipo Yowabu anatumiza amithenga kwa Davide kukanena kuti, “Ine ndamenyana ndi Raba ndipo ndatenga zitsime zake za madzi. Onani mutuwo |