2 Samueli 12:16 - Buku Lopatulika16 Chifukwa chake Davide anapempherera mwanayo kwa Mulungu; Davide nasala kudya, nalowa, nagona usiku wonse pansi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201416 Chifukwa chake Davide anapempherera mwanayo kwa Mulungu; Davide nasala kudya, nalowa, nagona usiku wonse pansi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa16 Nchifukwa chake Davide adapempherera mwanayo kwa Mulungu. Adaleka kudya, nakaloŵa m'nyumba, nkukagona pansi usiku wonse. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero16 Davide anapempherera mwanayo kwa Mulungu. Iye anasala chakudya ndipo analowa mʼnyumba mwake nagona pansi usiku wonse. Onani mutuwo |