2 Samueli 11:5 - Buku Lopatulika5 Ndipo mkaziyo anaima, natumiza munthu nauza Davide, kuti Ndili ndi pakati. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Ndipo mkaziyo anaima, natumiza munthu nauza Davide, kuti Ndili ndi pakati. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Kenaka ataona kuti waima, adatumiza mau kwa Davide kukamuuza kuti, “Inetu ndi mommuja, sindili bwino!” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Mkaziyo anakhala woyembekezera ndipo anatumiza mawu kwa Davide kunena kuti, “Ine ndine woyembekezera.” Onani mutuwo |