Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




2 Samueli 11:22 - Buku Lopatulika

22 Chomwecho mthengawo unamuka, nufika, nudziwitsa Davide zonse Yowabu anamtumiza.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

22 Chomwecho mthengawo unamuka, nufika, nudziwitsa Davide zonse Yowabu anamtumiza.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

22 Wamthenga uja adapita, nakafika kwa Davide, nakamuuza zonse zimene Yowabu adamuuza kuti akanene.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

22 Mthengayo ananyamuka, ndipo atafika anamuwuza Davide zonse zimene Yowabu anamutuma kuti akanene.

Onani mutuwo Koperani




2 Samueli 11:22
2 Mawu Ofanana  

Ndani anakantha Abimeleki mwana wa Yerubeseti? Sadamponyera kodi mphero mkazi wa palinga nafa iye ku Tebezi? Munasendera bwanji pafupi potere pa lingalo? Tsono udzanena, Mnyamata wanu Uriya Muhiti, iyenso adafa.


Ndipo mthengawo unati kwa Davide, Anthuwo anatipambana natulukira kwa ife kumundako, koma tinawagwera kufikira polowera kuchipata.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa