Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




2 Samueli 11:23 - Buku Lopatulika

23 Ndipo mthengawo unati kwa Davide, Anthuwo anatipambana natulukira kwa ife kumundako, koma tinawagwera kufikira polowera kuchipata.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

23 Ndipo mthengawo unati kwa Davide, Anthuwo anatilaka natulukira kwa ife kumundako, koma tinawagwera kufikira polowera kuchipata.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

23 Adauza Davide kuti, “Adani athu adaatipambana, ndipo adaatuluka kukalimbana nafe ku thengo. Koma ife tidaŵabweza mpaka ku khomo lakuchipata.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

23 Mthengayo anati kwa Davide, “Anthuwo anatiposa mphamvu ndipo anabwera kudzalimbana nafe poyera, koma ife tinawabwezera ku chipata cha mzindawo.

Onani mutuwo Koperani




2 Samueli 11:23
2 Mawu Ofanana  

Chomwecho mthengawo unamuka, nufika, nudziwitsa Davide zonse Yowabu anamtumiza.


Ndipo akuponyawo amene anali palinga anaponya anyamata anu; ndipo anyamata ena a mfumu anafa, ndi mnyamata wanu Uriya Muhiti, iyenso anafa.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa