2 Samueli 1:5 - Buku Lopatulika5 Ndipo Davide ananena ndi mnyamata wakumuuza, Udziwa bwanji kuti Saulo ndi Yonatani mwana wake anafa? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Ndipo Davide ananena ndi mnyamata wakumuuza, Udziwa bwanji kuti Saulo ndi Yonatani mwana wake anafa? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Apo Davide adamufunsa mnyamatayo kuti, “Iwe wadziŵa bwanji kuti Saulo ndi Yonatani nawonso adafa?” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Ndipo Davide anati kwa mnyamata amene anabweretsa nkhaniyi, “Ukudziwa bwanji kuti Sauli ndi mwana wake Yonatani afa?” Onani mutuwo |