Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




2 Samueli 1:25 - Buku Lopatulika

25 Ha! Amphamvuwo anagwa pakati pa nkhondo! Yonatani anaphedwa pamisanje pako.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

25 Ha! Amphamvuwo anagwa pakati pa nkhondo! Yonatani anaphedwa pamisanje pako.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

25 “Ha! Kani amphamvu agwa motere! Yonatani ali gone, atafa pa zitunda zako zachipembedzo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

25 “Taonani amphamvu agwa ku nkhondo! Yonatani wagona ataphedwa ku zitunda.

Onani mutuwo Koperani




2 Samueli 1:25
6 Mawu Ofanana  

Ulemerero wako, Israele, unaphedwa pa misanje yako. Ha! Adagwa amphamvu!


Ana aakazi inu a Israele, mulirire Saulo, amene anakuvekani ndi zofiira zokometsetsa, amene anaika zokometsetsa zagolide pa zovala zanu.


Ha! Amphamvuwo anagwa, ndi zida za nkhondo zinaonongeka.


Korona wagwa pamutu pathu; kalanga ife! Pakuti tinachimwa.


Zebuloni ndiwo anthu anataya moyo wao mpaka imfa, Nafutali yemwe poponyana pamisanje.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa