2 Samueli 1:18 - Buku Lopatulika18 nawauza aphunzitse ana Ayuda nyimbo iyi ya Uta, onani inalembedwa m'buku la Yasara, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201418 nawauza aphunzitse ana Ayuda nyimbo iyi ya Uta, onani inalembedwa m'buku la Yasara, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa18 Ndipo adalamula kuti mau a madandaulowo aŵaphunzitse kwa anthu a ku Yuda. Mau ake ndi aŵa, monga adalembedwera m'buku la Yasara. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero18 Ndipo analamula kuti anthu a ku Yuda aphunzitsidwe nyimbo ya maliroyi imene yalembedwa mʼbuku la Yasari: Onani mutuwo |