Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




2 Samueli 1:17 - Buku Lopatulika

17 Ndipo Davide analirira Saulo ndi Yonatani mwana wake ndi nyimbo iyi ya maliro;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

17 Ndipo Davide analirira Saulo ndi Yonatani mwana wake ndi nyimbo iyi ya maliro;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

17 Choncho Davide adaimba nyimbo ya madandaulo, kulira Saulo ndi Yonatani mwana wake.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

17 Davide anayimba nyimbo iyi ya maliro, kulira Sauli ndi mwana wake Yonatani.

Onani mutuwo Koperani




2 Samueli 1:17
7 Mawu Ofanana  

Ndipo pamene anthu okhala m'dzikomo, Akanani, anaona maliro a m'dwale la Atadi, anati, Awa ndi maliro aakulu a Aejipito: chifukwa chake dzina la pamenepo linatchedwa Abele-Mizraimu, pali tsidya lija la Yordani.


Ulemerero wako, Israele, unaphedwa pa misanje yako. Ha! Adagwa amphamvu!


Ndipo mfumu inanenera Abinere nyimbo iyi ya maliro, niti, Kodi Abinere anayenera kufa ngati chitsiru?


Ndipo Yeremiya anamlembera Yosiya nyimbo yomlira; ndi oimbira onse, amuna ndi akazi, amanena za Yosiya nyimbo za maliro zao mpaka lero lino; naziika zikhale lemba mu Israele; taonani, zilembedwa mu Nyimbo za Maliro.


Ndakhala ine monga ngati iye anali bwenzi langa, kapena mbale wanga; polira ndinaweramira pansi, monga munthu wakulira maliro amai wake.


Iyi ndi nyimbo ya maliro adzalira nayo, ana aakazi a amitundu adzachita nayo maliro; adzalirira nayo Ejipito ndi aunyinji ake onse, ati Ambuye Yehova.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa