2 Samueli 1:17 - Buku Lopatulika17 Ndipo Davide analirira Saulo ndi Yonatani mwana wake ndi nyimbo iyi ya maliro; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201417 Ndipo Davide analirira Saulo ndi Yonatani mwana wake ndi nyimbo iyi ya maliro; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa17 Choncho Davide adaimba nyimbo ya madandaulo, kulira Saulo ndi Yonatani mwana wake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero17 Davide anayimba nyimbo iyi ya maliro, kulira Sauli ndi mwana wake Yonatani. Onani mutuwo |