2 Mbiri 3:1 - Buku Lopatulika1 Pamenepo Solomoni anayamba kumanga nyumba ya Yehova ku Yerusalemu, m'phiri la Moriya, kumene Mulungu anaonekera kwa Davide atate wake pamalo pamene Davide anakonzeratu pa dwale la Orinani Myebusi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Pamenepo Solomoni anayamba kumanga nyumba ya Yehova ku Yerusalemu, m'phiri la Moriya, kumene Mulungu anaonekera kwa Davide atate wake pamalo pamene Davide anakonzeratu pa dwale la Orinani Myebusi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Tsono Solomoni adayambapo kumanga Nyumba ya Chauta ku Yerusalemu pa phiri la Moriya, pamene Chauta adaaonekera Davide bambo wake, pa malo omwe Davide adaaloza, pa bwalo lopunthira tirigu la Orinani Myebusi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Pamenepo Solomoni anayamba kumanga Nyumba ya Yehova mu Yerusalemu pa Phiri la Moriya, pamene Yehova anaonekera Davide abambo ake. Panali pabwalo lopunthirapo tirigu la Arauna Myebusi, malo amene anapereka Davide. Onani mutuwo |