Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




2 Mbiri 3:2 - Buku Lopatulika

2 Nayamba kumanga tsiku lachiwiri la mwezi wachiwiri, chaka chachinai cha ufumu wake.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

2 Nayamba kumanga tsiku lachiwiri la mwezi wachiwiri, chaka chachinai cha ufumu wake.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

2 Solomoniyo adayamba kumanga pa mwezi wachiŵiri wa chaka chachinai cha ufumu wake.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

2 Iye anayamba kumanga pa tsiku lachiwiri la mwezi wachiwiri mʼchaka chachinayi cha ulamuliro wake.

Onani mutuwo Koperani




2 Mbiri 3:2
3 Mawu Ofanana  

Ndipo kunachitika zitapita zaka mazana anai mphambu makumi asanu ndi atatu atatuluka ana a Israele m'dziko la Ejipito, chaka chachinai chakukhala Solomoni mfumu ya Israele, m'mwezi wa Zivi, ndiwo mwezi wachiwiri, iye anayamba kumanga nyumba ya Yehova.


Pamenepo Solomoni anayamba kumanga nyumba ya Yehova ku Yerusalemu, m'phiri la Moriya, kumene Mulungu anaonekera kwa Davide atate wake pamalo pamene Davide anakonzeratu pa dwale la Orinani Myebusi.


Ndipo maziko adawaika Solomoni akumangapo nyumba ya Mulungu ndi awa: utali wake, kuyesa mikono monga mwa muyeso wakale, ndiwo mikono makumi asanu ndi limodzi, ndi kupingasa kwake mikono makumi awiri.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa