2 Mbiri 3:2 - Buku Lopatulika2 Nayamba kumanga tsiku lachiwiri la mwezi wachiwiri, chaka chachinai cha ufumu wake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Nayamba kumanga tsiku lachiwiri la mwezi wachiwiri, chaka chachinai cha ufumu wake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Solomoniyo adayamba kumanga pa mwezi wachiŵiri wa chaka chachinai cha ufumu wake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Iye anayamba kumanga pa tsiku lachiwiri la mwezi wachiwiri mʼchaka chachinayi cha ulamuliro wake. Onani mutuwo |