2 Mbiri 2:9 - Buku Lopatulika9 ndiko kundikonzera mitengo yambirimbiri; pakuti nyumbayi nditi ndiimange idzakhala yaikulu ndi yodabwitsa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 ndiko kundikonzera mitengo yambirimbiri; pakuti nyumbayi nditi ndiimange idzakhala yaikulu ndi yodabwitsa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 kuti andidulire mitengo yochuluka, popeza kuti nyumba imene ndimangeyo idzakhala yaikulu ndi yochititsa kaso. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 kuti andipatse matabwa ambiri, chifukwa Nyumba imene ndikumanga iyenera kukhala yayikulu ndi yokongola. Onani mutuwo |