Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




2 Mbiri 2:2 - Buku Lopatulika

2 Nawerenga Solomoni amuna zikwi khumi mphambu makumi asanu ndi limodzi osenza mirimo, ndi amuna zikwi makumi asanu ndi atatu otema mitengo m'mapiri, ndi zikwi zitatu mphambu mazana asanu ndi limodzi kuwayang'anira.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

2 Nawerenga Solomoni amuna zikwi khumi mphambu makumi asanu ndi limodzi osenza mirimo, ndi amuna zikwi makumi asanu ndi atatu otema mitengo m'mapiri, ndi zikwi zitatu mphambu mazana asanu ndi limodzi kuwayang'anira.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

2 Tsono adalemba anthu 70,000 osenza katundu, anthu 80,000 okakumba miyala ku dziko lamapiri, ndiponso akapitao 3,600, oyang'anira anthuwo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

2 Iye analemba ntchito anthu 70,000 onyamula katundu ndi anthu 80,000 okumba miyala ku mapiri ndiponso akapitawo 3,600 oyangʼanira anthuwo.

Onani mutuwo Koperani




2 Mbiri 2:2
4 Mawu Ofanana  

Ndipo Huramu mfumu ya Tiro anatumiza mithenga kwa Davide, ndi mikungudza, ndi amisiri omanga miyala, ndi amatabwa, kuti ammangire nyumba.


Ndipo anaika zikwi makumi asanu ndi awiri za iwowa asenze mirimo, ndi zikwi makumi asanu ndi atatu ateme m'mapiri, ndi akapitao zikwi zitatu mphambu mazana asanu ndi limodzi agwiritse anthu ntchito.


Ndipo akalonga ananena nao, Akhale ndi moyo; ndipo anasanduka akutema nkhuni, ndi otungira madzi msonkhano wonse; monga akalonga adanena nao.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa