2 Mbiri 2:1 - Buku Lopatulika1 Ndipo Solomoni anati alimangire dzina la Yehova nyumba, ndiponso nyumba ya ufumu wake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Ndipo Solomoni anati alimangire dzina la Yehova nyumba, ndiponso nyumba ya ufumu wake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Tsono Solomoni adatsimikiza zoti amange nyumba yopembedzeramo Chauta ndiponso nyumba yaufumu ya iye mwini. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Solomoni anatsimikiza zoti amange Nyumba ya Dzina la Yehova ndi nyumba yake yaufumu. Onani mutuwo |