2 Mbiri 17:3 - Buku Lopatulika3 Ndipo Yehova anali ndi Yehosafati, popeza anayenda m'njira zake zoyamba za kholo lake Davide, osafuna Abaala; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Ndipo Yehova anali ndi Yehosafati, popeza anayenda m'njira zake zoyamba za kholo lake Davide, osafuna Abaala; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Chauta anali naye Yehosafati, chifukwa chakuti ankatsata makhalidwe oyambayamba aja a Asa bambo wake. Sadatsate Abaala, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Yehova anali ndi Yehosafati chifukwa mʼzaka zoyambirira anatsatira makhalidwe a Davide abambo ake. Iye sanafunsire kwa Abaala. Onani mutuwo |