2 Mbiri 17:4 - Buku Lopatulika4 koma anafuna Mulungu wa kholo lake nayenda m'malamulo ake, osatsata machitidwe a Israele. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 koma anafuna Mulungu wa kholo lake nayenda m'malamulo ake, osatsata machitidwe a Israele. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 koma ankatsata Mulungu wa atate ake, ndipo ankasunga malamulo ake, osatsata makhalidwe a Aisraele. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Koma anafunafuna Mulungu wa abambo ake ndipo anatsatira malamulo ake osati zochita za Israeli. Onani mutuwo |