Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




2 Mbiri 17:2 - Buku Lopatulika

2 Naika ankhondo m'mizinda yonse yamalinga ya Yuda, naika aboma m'dziko la Yuda, ndi m'mizinda ya Efuremu, imene adailanda Asa atate wake.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

2 Naika ankhondo m'midzi yonse yamalinga ya Yuda, naika aboma m'dziko la Yuda, ndi m'midzi ya Efuremu, imene adailanda Asa atate wake.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

2 Adaika magulu ankhondo ku mizinda yonse yamalinga ya ku Yuda, ndipo adamanga maboma ankhondo ku dziko la Yuda ndi ku mizinda ya ku Efuremu, imene Asa bambo wake adailanda.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

2 Iye anayika magulu a asilikali mʼmizinda yonse yotetezedwa ya Yuda, ndipo anamanga maboma mu Yuda ndi mʼmizinda yonse ya Efereimu imene Asa abambo ake analanda.

Onani mutuwo Koperani




2 Mbiri 17:2
6 Mawu Ofanana  

Ndipo Rehobowamu anakhala mu Yerusalemu, namanga mizinda yolimbikiramo mu Yuda.


Ndipo Abiya analondola Yerobowamu, namlanda mizinda yake, Betele ndi midzi yake, ndi Yesana ndi midzi yake, ndi Efuroni ndi midzi yake.


Ndipo pakumva Asa mau awa, ndi chinenero cha Odedi mneneriyo, analimbika mtima, nachotsa zonyansazo m'dziko lonse la Yuda ndi Benjamini, ndi m'mizinda adailanda ku mapiri a Efuremu; nakonza guwa la nsembe la Yehova lokhala pakhomo pachipinda cholowera cha nyumba ya Yehova.


Ndiwo amene analindirira mfumu, osawerenga iwo aja mfumu adawaika m'mizinda yamalinga mu Yuda monse.


Ndipo Yehova anali ndi Yehosafati, popeza anayenda m'njira zake zoyamba za kholo lake Davide, osafuna Abaala;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa