2 Mbiri 13:3 - Buku Lopatulika3 Ndipo Abiya anayambana nkhondo ali ndi khamu la ngwazi za nkhondo, amuna osankhika zikwi mazana anai; Yerobowamu atandandalitsa nkhondo yake ilimbane naye ndi amuna osankhika zikwi mazana asanu ndi atatu, ndiwo ngwazi zamphamvu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Ndipo Abiya anayambana nkhondo ali ndi khamu la ngwazi za nkhondo, amuna osankhika zikwi mazana anai; Yerobowamu atandandalitsa nkhondo yake ilimbane naye ndi amuna osankhika zikwi mazana asanu ndi atatu, ndiwo ngwazi zamphamvu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Abiya adanyamuka kupita ku nkhondo atatenga gulu lake la ankhondo olimba mtima okwanira 400,000 osankhidwa. Yerobowamu adandanditsa ankhondo ake oti amenyane ndi Abiya, anthu okwanira 800,000, amphamvu ndi osankhidwa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Abiya anapita ku nkhondo ndi asilikali odziwa bwino nkhondo 400,000, ndipo Yeroboamu anandandalitsa ankhondo, asilikali 800,000 odziwa bwino nkhondo, osankhidwa ndi amphamvu, woti amenyane naye. Onani mutuwo |