2 Mbiri 13:2 - Buku Lopatulika2 Anakhala mfumu m'Yerusalemu zaka zitatu; ndi dzina la make ndiye Mikaya mwana wamkazi wa Uriyele wa ku Gibea. Ndipo panali nkhondo pakati pa Abiya ndi Yerobowamu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Anakhala mfumu m'Yerusalemu zaka zitatu; ndi dzina la make ndiye Mikaya mwana wamkazi wa Uriyele wa ku Gibea. Ndipo panali nkhondo pakati pa Abiya ndi Yerobowamu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Adakhala mfumu mu Yerusalemu zaka zitatu. Mai wake anali Maaka, mwana wa Uriyele wa ku Gibea. Tsono panali nkhondo pakati pa Abiya ndi Yerobowamu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 ndipo analamulira mu Yerusalemu kwa zaka zitatu. Dzina la amayi ake linali Maaka mwana wa Urieli wa ku Gibeya. Koma panali nkhondo pakati pa Abiya ndi Yeroboamu. Onani mutuwo |