Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




2 Mafumu 9:4 - Buku Lopatulika

4 Pamenepo mnyamatayo, ndiye mneneri, anamuka ku Ramoti Giliyadi.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

4 Pamenepo mnyamatayo, ndiye mneneri, anamuka ku Ramoti Giliyadi.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

4 Motero mneneriyo adapita ku Ramoti-Giliyadi.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

4 Choncho mneneri wachinyamatayo anapita ku Ramoti Giliyadi.

Onani mutuwo Koperani




2 Mafumu 9:4
3 Mawu Ofanana  

Benigebere ku Ramoti Giliyadi, iyeyo anali nayo mizinda ya Yairi mwana wa Manase ili mu Giliyadiyo, iye anali nalo dziko la Arigobu lili mu Basani, mizinda yaikulu makumi asanu ndi limodzi yamalinga ndi zitseko zamkuwa;


Ndipo Elisa mneneriyo anaitana mmodzi wa ana a aneneri, nanena naye, Udzimangire m'chuuno, nutenge nsupa iyi ya mafuta m'dzanja mwako, numuke ku Ramoti Giliyadi.


Nalowa, ndipo taonani, akazembe a khamu alikukhala pansi; nati iye, Ndili ndi mau kwa inu, kazembe. Nati Yehu, Kwa yani wa ife tonse? Nati iye, Kwa inu, kazembe.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa