2 Mafumu 9:5 - Buku Lopatulika5 Nalowa, ndipo taonani, akazembe a khamu alikukhala pansi; nati iye, Ndili ndi mau kwa inu, kazembe. Nati Yehu, Kwa yani wa ife tonse? Nati iye, Kwa inu, kazembe. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Nalowa, ndipo taonani, akazembe a khamu alikukhala pansi; nati iye, Ndili ndi mau kwa inu, kazembe. Nati Yehu, Kwa yani wa ife tonse? Nati iye, Kwa inu, kazembe. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Atafika, adapeza atsogoleri ankhondo ali pa msonkhano. Tsono iyeyo adati, “Zikomo bwana, ine ndili ndi mau oti ndikuuzeni.” Yehu adafunsa kuti, “Kodi ukunena yani mwa ifeyo?” Mneneri uja adayankha nati, “Inuyo bwana.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Atafika ku Giliyadiko anapeza atsogoleri a ankhondo ali pa msonkhano. Iye anati, “Mtsogoleri, ine ndili ndi uthenga wanu.” Ndipo Yehu anafunsa kuti, “Uthengawo ndi wa yani pakati pathu?” Mneneriyo anayankha kuti, “Ndi wa inuyo, mtsogoleri.” Onani mutuwo |