2 Mafumu 9:3 - Buku Lopatulika3 Nutenge nsupa ya mafutayo, nuwatsanulire pamutu pake, nunene, Atero Yehova, Ndakudzoza iwe ukhale mfumu pa Israele. Utatero, tsegula pakhomo, nuthawe osachedwa, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Nutenge nsupa ya mafutayo, nuwatsanulire pamutu pake, nunene, Atero Yehova, Ndakudzoza iwe ukhale mfumu pa Israele. Utatero, tsegula pakhomo, nuthawe osachedwa, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Tsono ukathire mafutaŵa pamutu pake, ndipo ukanene kuti, ‘Chauta akukudzoza kuti ukhale mfumu ya ku Israele.’ Pomwepo ukatsekule chitseko ndipo ukathaŵe, usakachedwe ai.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Ndipo ukatenge botololi ndi kuthira mafuta pa mutu wake ndipo ukanene kuti, ‘Yehova akuti, Ine ndikudzoza iwe kukhala mfumu ya Israeli.’ Kenaka ukatsekule chitseko ndi kuthawa ndipo usakachedwe!” Onani mutuwo |