2 Mafumu 9:2 - Buku Lopatulika2 Ndipo ukafikako, ukaunguzeko Yehu mwana wa Yehosafati mwana wa Nimisi, nulowe numnyamukitse pakati pa abale ake, nupite naye ku chipinda cham'katimo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Ndipo ukafikako, ukaunguzeko Yehu mwana wa Yehosafati mwana wa Nimisi, nulowe numnyamukitse pakati pa abale ake, nupite naye ku chipinda cham'katimo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Ukakafika, ukafunefune Yehu, mwana wa Yehosafati, mdzukulu wa Nimisi. Utampeza ukamuuze kuti achokepo pakati pa anzake, ndipo ukaloŵe naye m'chipinda cham'kati. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Ukakafika kumeneko, ukafunefune Yehu mwana wa Yehosafati, mwana wa Nimisi. Ukapite kwa iye, ukamuchotse pakati pa anzake ndi kukamulowetsa mʼchipinda chamʼkati. Onani mutuwo |