2 Mafumu 9:1 - Buku Lopatulika1 Ndipo Elisa mneneriyo anaitana mmodzi wa ana a aneneri, nanena naye, Udzimangire m'chuuno, nutenge nsupa iyi ya mafuta m'dzanja mwako, numuke ku Ramoti Giliyadi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Ndipo Elisa mneneriyo anaitana mmodzi wa ana a aneneri, nanena naye, Udzimangire m'chuuno, nutenge nsupa iyi ya mafuta m'dzanja mwako, numuke ku Ramoti Giliyadi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Masiku amenewo Elisa adaitana mmodzi wa m'gulu la aneneri, namuuza kuti, “Konzekera ulendo ndipo utenge nsupa iyi ya mafuta m'manja, upite ku Ramoti-Giliyadi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Mneneri Elisa anayitanitsa mmodzi mwa ana a aneneri, namuwuza kuti, “Manga lamba mʼchiwuno mwako, tenga botolo la mafuta mʼdzanja lako ndipo upite ku Ramoti Giliyadi. Onani mutuwo |