2 Mafumu 8:4 - Buku Lopatulika4 Koma mfumu inalikulankhula ndi Gehazi mnyamata wa munthu wa Mulungu, ndi kuti, Ndifotokozere zazikulu zonse Elisa wazichita. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Koma mfumu inalikulankhula ndi Gehazi mnyamata wa munthu wa Mulungu, ndi kuti, Ndifotokozere zazikulu zonse Elisa wazichita. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Atafika kwa mfumu, adapeza mfumuyo ikulankhula ndi Gehazi, mtumiki wa munthu wa Mulungu uja, nimafunsa kuti, “Tandiwuza zonse zikuluzikulu zimene Elisa wachita.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Ndipo mfumu inkayankhula ndi Gehazi, mtumiki wa munthu wa Mulungu kuti, “Tandiwuza zinthu zikuluzikulu zimene Elisa wachita.” Onani mutuwo |
Koma Elisa anakhala pansi m'nyumba mwake, ndi akulu anakhala pansi pamodzi naye; ndipo mfumu inatuma munthu amtsogolere, koma asanafike kwa Elisa mthengayo, anati kwa akulu, Mwapenya kodi m'mene mwana uyu wambanda watumiza munthu kuchotsa mutu wanga? Taonani, pakufika mthengayo mutseke pakhomo, mumkankhe ndi chitseko. Kodi mapazi a mbuye wake samveka dididi pambuyo pake?