2 Mafumu 7:7 - Buku Lopatulika7 Nanyamuka, nathawa kuli sisiro, nasiya mahema ao, ndi akavalo ao, ndi abulu ao, misasa ili chimangire; nathawa apulumutse moyo wao. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Nanyamuka, nathawa kuli sisiro, nasiya mahema ao, ndi akavalo ao, ndi abulu ao, misasa ili chimangire; nathawa apulumutse moyo wao. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Motero adathaŵa ndi chisisila, nasiya mahema, akavalo, abulu ndiponso katundu wao yense monga momwe adaaliri, nathaŵa kuti apulumutse moyo wao. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Choncho ananyamuka nathawa ndi kachisisira ndipo anasiya matenti, akavalo ndi abulu awo. Iwo anasiya msasa wawo momwe unalili nathawa kupulumutsa miyoyo yawo. Onani mutuwo |